2 Samuel 8:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zadoki, mwana wa Ahitubi, ndiponso Ahimeleki, mwana wa Abiyatara, anali ansembe, ndipo Seraya anali mlembi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi Zadoki mwana wa Ahitubi, ndi Ahimeleki mwana wa Abiyatara anali ansembe, ndi Seraya anali mlembi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zadoki mwana wa Ahitubi ndi Ahimeleki mwana wa Abiatara anali ansembe; Seraya anali mlembi;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi Zadoki mwana wa Ahitubi, ndi Ahimeleki mwana wa Abyatara anali ansembe, ndi Seraya anali mlembi.