2 Samuel 8:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Benaya, mwana wa Yehoyada, anali nduna yoyang'anira Akereti ndi Apeleti, ndipo ana a Davide anali ansembe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Benaya mwana wa Yehoyada anayang'anira Akereti ndi Apeleti. Ndipo ana a Davide anali ansembe ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Benaya mwana wa Yehoyada anali mtsogoleri wa Akereti ndi Apeleti; ndipo ana a Davide anali ansembe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Benaya mwana wa Jehoyada anayang'anira Akereti ndi Apeleti. Ndipo ana a Davide anali nduna zace.