2 Thessalonians 1:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
pa tsiku limene Iye adzabwera kuti alemekezedwe mwa oyera, ndipo alandire ulemu mwa onse omkhulupirira. Ndipotu inunso mudzakhala nawo, chifukwa mudakhulupirira umboni wathu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamene adzadza kudzalemekezedwa mwa oyera mtima ake, ndi kukhala wodabwizitsa mwa onse akukhulupirira (popeza munakhulupirira umboni wathu wa kwa inu) m'tsiku lija.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pa tsiku limene iye adzabwera kudzalemekezedwa mwa oyera mtima ndi kuyamikidwa ndi onse amene anakhulupirira. Inu mudzakhala nawo mʼgulumo chifukwa munakhulupirira umboni wathu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamene adzadza kudzalemekezedwa mwa oyera mtima ace, ndi kukhala wodabwizitsa mwa onse akukhulupirira (popeza munakhulupirira umboni wathu wa kwa inu) m'tsiku lija.