2 Timothy 2:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono iwe, mwana wanga, limbika pakugwiritsa ntchito mphatso zaulere zimene uli nazo mwa Khristu Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwe, mwana wanga, limbika m'chisomo cha m'Khristu Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono iwe, mwana wanga, limbika mʼchisomo chimene chili mwa Khristu Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwe, mwana wanga, limbika m'cisomo ca m'Kristu Yesu.