2 Timothy 2:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Uzikana matsutsano opusa ndi opanda nzeru, paja ukudziŵa kuti zotere zimautsa mikangano.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mafunso opusa ndi opanda malango upewe, podziwa kuti abala ndeu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ukane matsutsano oyipa ndi opusa, chifukwa amayambitsa mikangano.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mafunso opusa ndi opanda malango upewe, podziwa kuti abala ndeu.