2 Timothy 2:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Umve nao zoŵaŵa monga msilikali wabwino wa Khristu Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Umve zowawa pamodzi nane monga msilikali wabwino wa Khristu Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Umve nane zowawa, monga msilikali wa Khristu Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Umve zowawa pamodzi nane monga msilikari wabwino wa Kristu Yesu.