2 Timothy 2:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa cha Uthenga Wabwinowu ndimamva zoŵaŵa, mpakanso kumangidwa m'ndende, ngati chigaŵenga. Koma mau a Mulungu sangathe kumangidwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
m'menemo ndimva zowawa kufikira zomangira, monga wochita zoipa; koma mau a Mulungu samangika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
umene ndikuwuvutikira choterewu mpaka kumangidwa ndi maunyolo ngati wakuba. Koma mawu a Mulungu sanamangidwe ndi maunyolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
m'menemo ndimva zowawa kufikira zomangira, monga wocita zoipa; koma mau a Mulungu samangika.