3 John 1:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikuyembekeza kudzakuwona posachedwa. Pamenepo tidzakambirana pakamwa mpakamwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndiyembekezera kufika kwanuko posachedwapa, ndipo tidzakambirana pamaso ndi pamaso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana, Mtendere ukhale nawe. Akulankhula abwenzi, Lankhula abwenzi ndi kuchula maina ao.