Acts 1:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Pali anthu ena amene akhala akutsagana nafe nthaŵi yonse pamene Ambuye Yesu anali pakati pathu,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero kuyenera kuti wina wa amunawo anatsatana nafe nthawi yonseyi Ambuye Yesu analowa natuluka mwa ife,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa chake ndi kofunika kusankha mmodzi wa anthu amene akhala nafe nthawi yonse imene Ambuye Yesu ankayenda nafe,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero kuyenera kuti wina wa amunawo anatsatana nafe nthawi yonseyi Ambuye Yesu analowa naturuka mwa ife,