Acts 11:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atumwi aja, ndiponso abale onse amene anali ku Yudeya, adamva kuti anthu a mitundu ina nawonso alandira mau a Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma atumwi ndi abale akukhala m'Yudeya anamva kuti amitundunso adalandira mau a Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atumwi ndi abale a ku Yudeya konse anamva kuti anthu a mitundu ina analandiranso Mawu a Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma atumwi ndi abale akukhala m'Yudeya anamva kuti amitundunso adalandira mau a Mulungu.