Acts 11:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo adati, “Inu mudaloŵa m'nyumba ya anthu osaumbalidwa, nkudya nawo pamodzi.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nanena kuti, Munalowa kwa anthu osadulidwa, ndi kudya nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo anati, “Iwe unalowa mʼnyumba ya anthu osachita mdulidwe ndi kudya nawo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nanena kuti, Munalowa kwa anthu osadulidwa, ndi kudya nao.