Acts 11:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ndidamva mau ondiwuza kuti, ‘Petro dzuka, ipha, udye.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinamvanso mau akunena ndi ine, Tauka Petro; ipha, nudye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kenaka ine ndinamva mawu akuti, ‘Petro, Imirira. Ipha, nudye.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinamvanso mau akunena ndi ine, Tauka Petro; ipha, nudye.