Acts 12:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pafupi ngati nthaŵi imeneyo mfumu Herode adagwira ena a mu Mpingo kuti aŵazunze.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma nyengo imeneyo Herode mfumu anathira manja ena a m'Mpingo kuwachitira zoipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inali nthawi yomweyi imene mfumu Herode anamanga ena a mu mpingo ndi cholinga chakuti awazunze.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma nyengo imeneyo Herode mfumu anathira manja ena a m'Eklesia kuwacitira zoipa.