Acts 12:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo adanena mokweza mau kuti, “Ameneŵa ndi mau a mulungu, osati a munthu ai.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anthu osonkhanidwawo anafuula, Ndiwo mau a Mulungu, si a munthu ai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthuwo anafuwula nati, “Amenewa ndi mawu a mulungu osati a munthu ayi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anthu osonkhanidwawo anapfuula, Ndiwo mau a Mulungu, si a munthu ai.