Acts 15:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene adadzipereka kuti atumikire Ambuye athu Yesu Khristu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
anthu amene anapereka moyo wao chifukwa cha dzina la Yesu Khristu Ambuye wathu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
anthu amene anapereka moyo wawo chifukwa cha dzina la Ambuye athu Yesu Khristu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
anthu amene anapereka moyo wao cifukwa ca dzina la Yesu Kristu Ambuye wathu.