Acts 15:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atakhala kumeneko nthaŵi ndithu, abale aja adaŵalola mwamtendere kuti abwerere kwa amene adaaŵatuma. [
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene anakhala nthawi, abale analawirana nao ndi mtendere amuke kwa iwo amene anawatumiza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atakhala kumeneko kwa kanthawi, abale aja anatsanzikana nawo mwamtendere kuti abwerere kwa amene anawatuma.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene anakhala nthawi, abale analawirana nao ndi mtendere amuke kwa iwo amene anawatumiza. [