Acts 15:39 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo iwo adakangana kwambiri, kotero kuti adapatukana. Barnabasi adamtenga Marko uja naloŵa m'chombo kupita ku Kipro.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panali kupsetsana mtima, kotero kuti analekana wina ndi mnzake; ndipo Barnabasi anatenga Marko, nalowa m'ngalawa, nanka ku Kipro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anatsutsana kwambiri kotero kuti anapatukana. Barnaba anatenga Marko ndipo anakwera sitima ya pamadzi kupita ku Kupro.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panali kupsetsana mtima, kotero kuti analekana wina ndi mnzace; ndipo Bamaba anatenga Marko, nalowa n'ngalawa, nanka ku Kupro.