Acts 16:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo woyang'anira ndende uja adaitanitsa nyale, nathamangira m'kati, ndipo ali njenjenje ndi mantha, adadzigwetsa ku mapazi a Paulo ndi Silasi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mdindo anaitanitsa nyali, natumphira m'kati, alinkunthunthumira ndi mantha, nagwa pamaso pa Paulo ndi Silasi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Woyangʼanira ndendeyo anayitanitsa nyale, nathamangira mʼkati ndipo anadzigwetsa pa mapazi a Paulo ndi Sila akunjenjemera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mdindo anaitanitsa nyali, natumphira m'kati, alinkunthunthunrlra ndi mantha, nagwa pamaso pa Paulo ndi Sila,