Acts 16:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene adafika ku malire a Misiya, adayesa kuloŵa m'dera la Bitiniya, koma Mzimu wa Yesu sadaŵalole.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamene anafika kundunji kwa Misiya, anayesa kunka ku Bitiniya; ndipo Mzimu wa Yesu sanawaloleza;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atafika ku malire a Musiya, anayesa kulowa ku Bituniya, koma Mzimu wa Yesu sunawalole kutero.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
anayesa kunka ku Bituniya; ndipo Mzimu wa Yesu sanawaloleza;