Acts 18:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti iye adaatsutsa Ayuda mwamphamvu pamaso pa anthu, natsimikiza ndi Malembo kuti Yesu ndiyedi Mpulumutsi wolonjezedwa uja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti ndi mphamvu anatsutsa Ayuda, pamaso pa anthu, nasonyeza mwa malembo kuti Yesu ndiye Khristu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti iye anatsutsa Ayuda mwamphamvu pamaso pa anthu, natsimikiza kuchokera mʼMalemba kuti Yesu ndiye Khristu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pakuti ndi mphamvu anatsutsa Ayuda, pamaso pa anthu, nasonyeza mwa malembo kuti Yesu ndiye Kristu.