Acts 19:41 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atanena zimenezi, adauza anthu aja kuti azipita.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene ananena izi, anamasula msonkhano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye atatha kunena zimenezi anawuza gulu la anthulo kuti libalalike.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene ananena izi, anamasula msonkhano.