Acts 19:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Okhulupirira aja atamva zimenezi, adabatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene anamva ichi, anabatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atamva zimenezi, anabatizidwa mʼdzina la Ambuye Yesu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene anamva ici, anabatizidwa m'dzina la Ambuye Yesu.