Acts 19:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo onse pamodzi analipo ngati khumi ndi aŵiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Onsewo anali ngati amuna khumi ndi awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu onsewo analipo khumi ndi awiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Onsewo anali ngati amuna khumi ndi awiri.