Acts 20:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tsopano ndikudziŵa kuti inu nonse amene ndidakuyenderani kumakulalikirani za ufumu wa Mulungu, simudzaonanso nkhope yanga ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tsopano, taonani, ndidziwa ine kuti inu nonse amene ndinapitapita mwa inu kulalikira ufumuwo, simudzaonanso nkhope yanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsopano ndikudziwa kuti inu nonse amene ndinakuyenderani ndi kumakulalikirani ufumu wa Mulungu simudzaonanso nkhope yanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tsopano, taonani, ndidziwa ine kuti inu nonse amene ndinapitapita mwa inu kulalikira ufumuwo, simudzaonanso nkhope yanga.