Acts 21:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono pamenepa titani? Kumva adzamva ndithu kuti mwafika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nchiyani tsono? Adzamva ndithu kuti wafika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nanga pamenepa ife titani? Iwo adzamva ndithu kuti iwe wabwera,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nciani tsono? adzamva ndithu kuti wafika.