Acts 21:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pompo iye adatenga asilikali ndi atsogoleri a magulu a asilikali, nathamangira anthu aja. Pamene anthuwo adaona mkulu wa asilikaliyo ndi asilikali aja, adaleka kummenya Paulo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo posachedwa iye anatenga asilikali ndi akenturiyo, nathamanga, nawatsikira; ndipo iwowa, pakuona kapitao wamkulu ndi asilikali, analeka kumpanda Paulo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi yomweyo iye anatenga asilikali ndi atsogoleri a magulu a asilikali ndi kuthamangira kumene kunali anthuwo. Anthuwo ataona mkuluyo ndi asilikali ake analeka kumenya Paulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo posacedwa iye anatenga asilikari ndi akenturiyo, nathamanga, nawatsikira; ndipo iwowa, pakuona kapitao wamkuru ndi asilikari, analeka kumpanda Paulo.