Acts 21:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo titatsazikana, ife tidakaloŵa m'chombo, iwowo nkumabwerera kwao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Titatsanzikana, tinalowa mʼsitima ija, iwowo anabwerera ku nyumba zawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao.