Acts 22:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndidati, ‘Zoonadi Ambuye, chifukwa iwo omwe akudziŵa kuti ine ndinkapita ku nyumba iliyonse yamapemphero kukaŵagwira ndi kuŵaponya m'ndende, nkumaŵakwapula onse okhulupirira Inu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinati ine, Ambuye, adziwa iwo okha kuti ndinali kuika m'ndende ndi kuwapanda m'masunagoge onse iwo akukhulupirira Inu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinayankha Ambuye kuti, “Anthu awa akudziwa kuti ine ndinkapita ku sunagoge iliyonse ndipo ndinkawaponya mʼndende ndi kuwakwapula amene ankakhulupirira inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinati ine, Ambuye, adziwa iwo okha kuti ndinali kuika m'ndende ndi kuwapanda m'masunagoge onse iwo akukhulupirira Inu;