Acts 22:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anzanga apaulendo adaakuwona kuŵalako, koma mau a amene ankalankhula naneyo sadaŵamve.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamva mau akulankhula nane.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anzanga a paulendo anaona kuwalako, koma sanamve mawuwo, a Iye amene amayankhula nane.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamva mau akulankhula nane.