Acts 23:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidapeza kuti ankamneneza chifukwa cha nkhani yokhudza Malamulo ao, koma osati mlandu womuphera kapena womuponyera m'ndende.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinapeza kuti adamnenera za mafunso a chilamulo chao; koma analibe kumnenera kanthu kakuyenera imfa kapena nsinga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinapeza kuti amamuyimba mlandu wa nkhani ya malamulo awo, koma panalibe mlandu woyenera kumuphera kapena kumuyika mʼndende.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinapeza kuti adamnenera za mafunso a cilamulo cao; koma analibe kumnenera kanthu kakuyenera imfa kapena nsinga.