Acts 23:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Paulo adamuuza kuti, “Mulungu adzatchaya iweyo, chipupa chopaka njeresawe! Iwe wakhala pamenepo kuti undiweruze potsata Malamulo a Mose, nanga bwanji ukuŵaphwanya Malamulowo pakulamula kuti anditchaye?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo Paulo anati kwa iye, Mulungu adzakupanda iwe, khoma loyeretsedwa iwe; ndipo kodi ukhala iwe wakundiweruza mlandu monga mwa chilamulo, ndipo ulamulira andipande ine posanga chilamulo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo Paulo anamuwuza kuti, “Mulungu adzakukantha, iwe munthu wachiphamaso! Wakhala pamenepo kuti undiweruze ine monga mwalamulo, koma iweyo ukuphwanya lamulolo polamulira kuti andimenye!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo Paulo anati kwa iye, Mulungu adzakupanda iwe, khoma loyeretsedwa iwe; ndipo kodi ukhala iwe wakundiweruza mlandu monga mwa cilamulo, ndipo ulamulira andipande ine posanga cilamulo?