Acts 23:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo amene adaaimirira pafupi adauza Paulo kuti, “Bwanji ukunena zachipongwe kwa mkulu wa ansembe wa Mulungu?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iwo akuimirirako anati, Ulalatira kodi mkulu wa ansembe wa Mulungu?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu amene anayimirira pafupi ndi Paulo anati, “Bwanji ukunyoza mkulu wa ansembe wa Mulungu?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iwo akuimirirako anati, Ulalatira kodi mkulu wa ansembe wa Mulungu?