Acts 24:7 — Compare Translations

2 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Lisiasi, mkulu wa asilikali, adadzamtsomphola kumanja kwathu mwankhondo,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma, mkulu wa asilikali Lusiya anafika mwamphamvu namuchotsa mʼmanja mwathu.