Acts 25:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine ndidaathedwa nzeru, osadziŵa kuti ndiifufuze bwanji nkhani imeneyi. Choncho ndidamufunsa Pauloyo ngati akadakonda kupita ku Yerusalemu kuti mlandu wakewo ukazengedwere kumeneko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ine posinkhasinkha za mafunso awa ndinamfunsa ngati afuna kupita ku Yerusalemu, ndi kuweruzidwa komweko za izi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinathedwa nzeru wosadziwa momwe ndikanafufuzira nkhaniyi; kotero ndinafunsa ngati akanafuna kupita ku Yerusalemu kuti akaweruzidwe kumeneko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ine posinkhasinkha za mafunso awa ndinamfunsa ngati afuna kupita ku Yerusalemu, ndi kuweruzidwa komweko za izi.