Acts 27:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sitidaone dzuŵa kapena nyenyezi masiku ambiri, koma namondwe ankakalipabe, mpaka tonse tidaatayiratu chikhulupiriro chakuti tipulumuka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo m'mene dzuwa kapena nyenyezi sizinatiwalira masiku ambiri, ndipo namondwe wosati wamng'ono anatigwera, chiyembekezo chonse chakuti tipulumuke chidatichokera pomwepo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sitinaone dzuwa kapena nyenyezi kwa masiku ambiri ndipo namondwe anapitirira kuwomba kwambiri, pomaliza ife tonse tinalibenso chiyembekezo choti nʼkupulumuka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo m'mene dzuwa kapena nyenyezi sizinatiwalira masiku ambiri, ndipo namondwe wosati wamng'ono anatigwera, ciyembekezo conse cakuti tipulumuke cidaticokera pomwepo.