Acts 27:35 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atanena zimenezi, Paulo adatenga buledi, nayamika Mulungu pamaso pa onse. Ndipo adamnyema bulediyo nayamba kudya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo atanena izi, ndi kutenga mkate, anayamika Mulungu pamaso pa onse; ndipo m'mene adaunyema anayamba kudya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Paulo atanena zimenezi, anatenga buledi nayamika Mulungu pamaso pa onse. Ndipo ananyema bulediyo nayamba kudya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo atanena izi, ndi kutenga mkate, anayamika Mulungu pamaso pa onse; ndipo m'mene adaunyema anayamba kudya.