Acts 28:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kumeneko tidapeza abale, ndipo adatiitana kuti tikhale nawo masiku asanu ndi aŵiri. Motero tidakafika ku Roma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamenepo tinakomana ndi abale, amene anatiumirira tikhale nao masiku asanu ndi awiri; ndipo potero tinafika ku Roma.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumeneko tinapezako abale amene anatiyitana kuti tikhale nawo sabata limodzi. Ndipo kenaka tinapita ku Roma.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamenepo tinakomana ndi abale, amene anatiumirira tikhale nao masiku asanu ndi awiri; ndipo potero tinafika ku Roma.