Acts 28:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma pamene Ayuda adakana, ndidakakamizidwa kupempha kuti mlandu wangawo ndidzagwade kwa Mfumu ya ku Roma kuno. Sikuti ndinali ndi kanthu konenezera mtundu wanga ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pakukanapo Ayuda, ndinafulumidwa mtima kutulukira kwa Kaisara; si kunena kuti ndinali nako kanthu kakunenera mtundu wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Ayuda atakana, ine ndinakakamizidwa kupempha kuti ndikaonekere pamaso pa Kaisara, sikuti ndinali ndi kanthu konenezera mtundu wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pakukanapo Ayuda, ndinafulumidwa mtima kuturukira kwa Kaisara; si kunena kuti ndinali nako kanthu kakunenera mtundu wanga.