Acts 28:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nkuwona ndakuitanani kuti ndilankhule nanu. Pakuti ndamangidwa ndi unyolo uwu chifukwa chokhulupirira chinthu chimene Aisraele akuyembekeza.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa cha ichi tsono ndinakupemphani inu mundione ndi kulankhula nane; pakuti chifukwa cha chiyembekezo cha Israele ndamangidwa ndi unyolo uwu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa chifukwa ichi ndapempha kuti ndionane nanu ndi kuyankhula nanu. Pakuti nʼchifukwa cha chiyembekezo cha Israeli ndamangidwa unyolo uwu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa ca ici tsono ndinakupemphani inu mundione ndi kulankhula nane; pakuti cifukwa ca ciyembekezo ca Israyeli ndamangidwa ndi unyolo uwu.