Acts 3:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu anali woyera mtima ndi wolungama, koma inu mudamkana, ndipo m'malo mwake mudapempha kuti akumasulireni chigaŵenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma inu munamukana Woyera ndi Wolungamayo ndipo munapempha kuti akumasulireni munthu wakupha anthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu,