Acts 3:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndiponso tsopano abale anga, ndikudziŵa kuti inu ndi akuluakulu anu mudachita zimenezi mosadziŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tsopano, abale, ndidziwa kuti munachichita mosadziwa, monganso akulu anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Tsopano abale ine ndikudziwa kuti inu munachita zimenezi mosadziwa, monga momwenso anachitira atsogoleri anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tsopano, abale, ndidziwa kuti munacicita mosadziwa, monganso akulu anu.