Acts 3:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ndipo adzakutumizirani Yesu uja amene adamusankhuliratu kuti akhale Mpulumutsi wanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo atume amene anaikidwa kwa inu, Khristu Yesu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndi kuti Iye atumize Yesu Khristu amene anasankhidwa chifukwa cha inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo atume amene anaikidwa kwa inu, Kristu Yesu;