Acts 3:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho Mulungu atasankhula Mtumiki wake adayamba kumtuma kwa inu, kuti akudalitseni pakuthandiza aliyense mwa inu kusiya njira zake zoipa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuyambira ndi inu, Mulungu, ataukitsa Mwana wake, anamtuma kukudalitsani inu, ndi kukubwezani yense ku zoipa zake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Mulungu anaukitsa mtumiki wake, anamutuma Iye poyamba kwa inu kuti akudalitseni pobweza aliyense wa inu ku zoyipa zake.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuyambira ndi inu, Mulungu, ataukitsa Mwana wace, anamtuma kukudalitsani inu, ndi kukubwezani yense ku zoipa zace.