Acts 3:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iye nkuŵayang'anadi namaganiza kuti alandira kanthu kwa iwo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iye anavomereza iwo, nalingirira kuti adzalandira kanthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthuyo anawayangʼanitsitsa kuyembekezera kuti alandira kanthu kuchokera kwa iwo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iye anabvomereza iwo, nalingirira kuti adzalandira kanthu.