Acts 5:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo mpingo wonse ndi anthu onse amene adamva zimenezi, adagwidwa ndi mantha aakulu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anadza mantha akulu pa Mpingo wonse, ndi pa onse akumva izi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mpingo wonse ndi anthu onse amene anamva zimenezi anachita mantha kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anadza mantha akuru pa Mpingo wonse, ndi pa onse akumvaizi.