Acts 5:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adagwira atumwi aja, naŵatsekera m'ndende ya Boma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nathira manja atumwi, nawaika m'ndende ya anthu wamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anagwira atumwi ndi kuwatsekera mʼndende ya anthu wamba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nathira manja atumwi, nawaika m'ndende ya anthu wamba.