Acts 5:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene abwalo aja adamva zimenezi, adakwiya kwambiri nafuna kuŵapha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma m'mene anamva iwo analaswa mtima, nafuna kuwapha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Akuluakuluwo atamva zimenezi anakwiya kwambiri nafuna kuwapha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma m'mene anamva iwo analaswa mtima, nafuna kuwapha.