Acts 5:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Petro adamufunsa kuti, “Tandiwuzani, kodi pogulitsa munda wanu, mtengo wake unali ndalama izi?” Maiyo adati, “Inde, mtengo wake unali womwewo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Petro ananena naye, Undiuze, ngati munagulitsa mundawo pa mtengo wakuti. Ndipo ananena, Inde, wakuti.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Petro anamufunsa iye kuti, “Tandiwuza, kodi izi ndi ndalama zonse zimene iwe ndi Hananiya munalandira mutagulitsa munda?” Mkaziyo anati, “Inde ndi zimenezo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Petro ananena naye, Undiuze, ngati munagulitsa mundawo pa mtengo wakuti. Ndipo ananena, Inde, wakuti.