Acts 6:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma adalephera kumgonjetsa, chifukwa iye ankalankhula ndi nzeru zochokera kwa Mzimu Woyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo sanathe kuilaka nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iwo sanathe kumugonjetsa chifukwa iye ankayankhula ndi nzeru zimene Mzimu Woyera anamupatsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo sanathe kuilaka nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye.