Acts 6:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ife tidzadzipereka ku ntchito ya kupemphera ndi kulalika mau a Mulungu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ife tidzalimbika m'kupemphera, ndi kutumikira mau.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ife tidzadzipereka kuti tizipemphera ndi kulalikira mawu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ife tidzalimbika m'kupemphera, ndi kutumikira mau.